Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 171
  • Nyimbo Yachilakiko

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nyimbo Yachilakiko
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kugonjetsa Dziko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Chitani Monga Amuna’
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 171

Nyimbo 171

Nyimbo Yachilakiko

(Eksodo 15:1)

1. ‘Imbirani Ya, chifukwa ali wokwezekadi.

Apakavalowo Wawamiza munyanja.

Ya ndimphamvu yangadi, Iye wandipulumutsa.

M’lungu wanga; Ndidzamutamanda.

Magaleta a Farao ndi gululo Wawaponyera m’nyanja.

Dzanja lanu lamanja Yehova Lamphamvudi muluso.’

2. Aisrayeli Anaimba za chilakikocho.

M’nthaŵi yathu ino Tiwona chilakiko.

Yesu alamulira, Dongosolo lidzandira.

Tikondwera, Ndi chipulumutso!

Chinjoka Satana, ndi angelo ake—Aponyedwa padziko.

Mwanawankhosayo alakika. Mdimawo wapitadi.

3. Tamandani Ya. Ulemelero ndi mphamvu nzake.

Ufumu wakhala, Kukantha nkhonya msanga.

Tiimba mofuula. Zikomo M’lungu ndi Yesu.

Achimwemwe Kukhala ndi moyo.

Kwa M’lungu wathu Yehova ndi Mesiya Timawayamikira.

Adzatipatsa chipulumutso. Nyimbo idzaimbidwa!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena