Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 60
  • Ufumu wa Mulungu wa Zaka Chikwi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ufumu wa Mulungu wa Zaka Chikwi
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Konzekerani Zaka Chikwi Zomwe Zili Zofunika!
    Nsanja ya Olonda—1999
  • Kulinganiza Tsopano Kaamba ka Zaka Chikwi Zikudzazo
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Kusankha Okhala ndi Phande mu Ulamuliro wa Dziko
    Boma Lathu la Dziko Likudza’lo—Ufumu wa Mulungu
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 60

Nyimbo 60

Ufumu wa Mulungu wa Zaka Chikwi

(Chivumbulutso 20:4-6)

1. M’lungu wati pakhale zaka chikwi.

Zoti Mwana wake alamule anthu.

Odzozedwa adzalamula naye.

Adzakhalatu mafumu ndi ansembe.

2. Nakomera mtima anthu onsewo,

Adzakondwa ndi ntchito yochotsa tchimo.

Paradaiso adzakuta dziko.

Owomboledwa onsewo atama Ya.

3. Zaka chikwi, mu Ufumu wa Kristu!

Ndi chikhulupiliro tikuziwona:

Oukawo aphunzira za M’lungu.

Ndi tsiku loweruza mu chilungamo.

4. Tiyenitu tiyesetse mwamphamvu;

Kukhala maso tsiku layandikira.

Molimba mtima tichite mwanzeru,

Kuitana onse kudza kwa Mulungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena