Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 179
  • Tiyenera Kuyembekezera Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiyenera Kuyembekezera Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mukhoza Kuyembekezera Moleza Mtima?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kristu Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woyang’anira Dera wa 2023-2024
  • “Sadzachedwa”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 179

Nyimbo 179

Tiyenera Kuyembekezera Yehova

(Aroma 8:19)

1. ‘Kagulu ka nkhosako.’

Kayembekezera Ya.

Adzachita ufumu;

Ayembekezeradi.

Kristu alamula;

Ali woyenera.

Adzapereka mphotho

Kwa anthu akewo

Olengeza ’Fumu.

2. Mabwenzi awo ndiwo

Khamu la “nkhosa zina.”

Onse chokhumba chawo

Ndikusunga umphumphu.

Kuŵala kukula

Adikilirabe

Kusonyezatu ana

Kodzetsa mtendere,

Indedi mtendere.

3. Ya walonjeza anthu

Za dziko latsopano.

Mokhala kulungama,

Pobadwa Ufumuwo.

Timalakalaka,

Pomwe tiphunzira.

Timadalira mwa Ya;

Timuyembekeze.

Timuyembekeze.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena