Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 217
  • Kupeza Ubwenzi wa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kupeza Ubwenzi wa Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova—Kodi Ndimnansi Wanu Kapena Bwenzi Lanu?
    Nsanja ya Olonda—1992
  • Mvetserani Mbiri ya Ufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mtundu Woyera wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 217

Nyimbo 217

Kupeza Ubwenzi wa Yehova

(Salmo 15:1, 2)

1. Ndani adzakhala bwenzi la Yehova?

Ndani adzakhala muhema wanu kosatha?

Iye wosawopa Wopanda tchimoyo,

Inde, woyera mtima nachita mowonadi.

Ubwenzi wanu Ya, mupatsa kwa yani?

Ndani adzakhala nanu muphiri loyera?

Iye wosamalira malankhulidwe ake kwa wina.

(Korasi)

2. Ndani adzakhala nanu O Mulungu?

Ndani angakhalitsetu monga bwenzi lanu?

Iye wowonayo, Ngakhale muvuto,

Ayenda molungama, nachita chowonadi.

Tikhumba ubwenzi wanutu Yehova.

Mawu anu atidziŵitsa zofuna zanu.

Tikonze njira zathu ndipo mukhalebe bwenzi lathu.

(Korasi)

3. Tifuna kukhala ndi inu Yehova.

Mtendere wanu uposa chidziŵitso chonse.

Mwa Ambuye Yesu, Munabwezeretsa

Kulambirako. Makamu akulambirani.

Wammwambamwambanu Tidzatchinjiriza

Ubwenzi wanu ndi kukhala wopanda banga.

Monga ogwirizana tidzaima paphiri lanulo.

(KORASI)

Tikhale mabwenzi Anu Ya kosatha.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena