Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 172
  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova
  • Muziika Ufumu Pamalo Oyamba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 172

Nyimbo 172

Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba

(Mateyu 6:33)

1. Kwa Yehova chokongola,

Ndi chomkondweretsadi,

Ndicho Ufumu wa Kristu,

Udzawongola zinthu.

Aneneri anawona

Nayembekezeradi.

Lero mtsogoleri

Yesu Amatilimbikitsa.

(Korasi)

2. Polalika Ufumuwo

Ndimwaŵi kwa ’nthu ake!

Tapatsidwatu ntchitoyo,

Tiisamaliredi.

Tikhala bwanji ndi nkhaŵa

Zofunika za maŵa?

M’lungu adzatigaŵira

Tikafuna Ufumu.

(Korasi)

3. Dongosololi lidzatha;

La M’lungu lidzayamba.

Anthu adzatama M’lungu;

Paradaiso adza.

Tifalitse za Ufumu,

Kwa anthu onga nkhosa

Kuyembekeza Yehova

Ndi Teokrase wake.

(KORASI)

Mufune Ufumu kaye

Ndi chilungamo cha Ya.

Mkwezeni iye choyamba,

Ndi kumtumikirabe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena