Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 105
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Ufumu wa Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Tamandani Mwana Woyamba Kubadwa wa Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 105

Nyimbo 105

Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!

(Ahebri 1:6)

1. Titame Woyambayo

—Woloŵatu nyumba—

Chilengedwere iye,

Amamvera M’lungu.

Anapanga zinthuzo

Zammwamba ndi m’dziko,

Monga womlankhulira,

Anena za M’lungu.

2. Pokhala ngati M’lungu,

Sanayese konse

Kupikisana naye

Mulungu wakeyo.

Koma nadzichepetsa

Nakhalatu munthu

Kukwezatu Yehova

Ndi kupatsa moyo.

3. Kristu anakwezedwa

Natukulidwadi

Kuimira Mulungu

Kuyeretsa dzina.

Adzatitchinjiriza

Pa Armagedopo,

Kuwononga adani,

Nadzetsa mtendere.

4. Tamatu Woyambayo!

Nena za Ufumu.

Lalikadi ponsepo;

Kunyumba ndi nyumba.

Mosamalitsa ndithu

Thandizatu ena.

Kuti atamandetu

Woyamba kubadwa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena