Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 194
  • Loŵani m’Mabwalo a Kachisi wa Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loŵani m’Mabwalo a Kachisi wa Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Malo Abwino a Yehova Olambiliramo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chilengedwe Chonse, Tamandani Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Ili ndi Lamulo Lokhudza Kachisi”
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Kulandira Mfumu Yakudzayo!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 194

Nyimbo 194

Loŵani m’Mabwalo a Kachisi wa Yehova!

(Salmo 100:4)

1. M’dziko lonse Mboni za Ya zikulalika:

‘M’lungu ndi Kristu alamulira!’

Ndinthaŵi yolambira Wamphamvuyonseyo,

Ndi kukhalabe munyumba yake.

2. Tsekulani zipata ofatsa aloŵe.

M’loŵe mkati, m’bwalo la Mulungu.

Mudze ndi mphatso kuphiri lake loyera.

Musangalale mumtima mwanu.

3. Tsikuli nloti ‘wamng’ono wakhala chikwi.’

“Nkhosa zina” zikuyandikira.

Ngati njiŵa aloŵa m’bwalo lakachisi

Mmene angalemekeze M’lungu.

4. Loŵani m’zipata ndi kutama Yehova.

Nchiitano chomveka konseko.

Msonkhane m’bwalo la kulambira kowona.

M’dzakhale mmenemo nthaŵi zonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena