Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 152
  • Kuyamikira Chifundo cha Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuyamikira Chifundo cha Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Tiyenera Kukhala Mtundu Wanji wa Anthu?
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Kondwerani m’Chiyembekezo’
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kumvera Mulungu Koposa Anthu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 152

Nyimbo 152

Kuyamikira Chifundo cha Mulungu

(Aroma 11:33-35)

1. Chuma, nzeru ndi kudziŵa

Zikhala ndi Mulungu!

Ali wosasanthulika!

Muziweruzo zake!

Kodi ife tamlangiza

Kapena kumthandiza,

Kukhala nafe mangaŵa

Kuti tibwezeredwe?

2. Ndichifundo cha

Yehova Tikhale oyamika

Kupereka kwa Mulungu

Matupi amoyowa.

Pokhala tadzipereka,

Tikhaletu owona,

Ndi kudziŵa kwathu konse

Tichite zothekera.

3. Osayenda mwa dzikoli,

Tikonze maganizo

Mwa mphamvu ya chowonadi

Ndi chikhulupiliro.

Mopemphera kosaleka,

Titumike mofatsa

Kusonyezana chikondi;

Tidzapeza mtendere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena