Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 207
  • Kodi Ndife a Yani?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ndife a Yani?
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ndife Anthu a Ndani?
    Imbirani Yehova
  • Kodi Ndife A Ndani
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Adzakulimbitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 207

Nyimbo 207

Kodi Ndife a Yani?

(1 Akorinto 6:20)

1. Ndinutu wa yani?

Mumamvera yani?

Amene mutumikira

Yemweyo ndi mbuye wanu.

Sungatumikire

Milungu iŵiri

Singagaŵane chikondi chako.

Sukhulupirika.

2. Ndinutu wa yani?

Mudzamvera yani?

Pakuti wina ngwonama,

Wina ngwowona; Sankhani.

Kodi Kaisara

Udzagonjera ’ye?

Kaya udzamveratu Mulungu

Ndi chifuno chake?

3. Ndinetu wa yani?

Ndidzamveratu Ya.

Ndidzatumikira Mlungu;

Wa chowonadi kosatha.

Anandigulatu;

Sindiri wa anthu.

Imfa ya Kristu ndi dipo langa;

Sindidzabwevuka.

4. Ndife a Mulungu!

Musakayikire.

Tikondwera ndi umodzi

Wonenedweratu kale.

Mongatu mafuta

Odzoza wansembe,

Timapeza ukoma kukhala

M’chowonadi chake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena