Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 166
  • Wonani Khamu la Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Wonani Khamu la Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova
    Imbirani Yehova
  • Ndife Gulu Lankhondo la Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • “Nkhosa Zosochera Ndidzazifunafuna”
    Bwererani kwa Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 166

Nyimbo 166

Wonani Khamu la Yehova!

(Yoweli 2:7)

1. Wonani khamulo,

La Yehovayo,

Lilengeza ’fumu

Wa Kristu Yesu.

Lipita mtsogolo,

Molimba mtima;

Lodalira M’lungu,

Lopanda mantha.

Lidalira M’lungu,

Potsata Kristu,

Lilalikirabe:

“Alamulira.”

2. Atumiki a Ya

Afuna “nkhosa”

Ziri mu Babulo

Ndipo zilira.

Ayesayesabe

Kuzimasula;

Aziitanira

Kumisonkhano.

Zitamasulidwa,

Ziphunzitsidwa

Kuzindikiratu

Zinthu zowona.

3. Tawonani ‘khamu

Lalikululo’,

Ndi ‘otsalirawo,’

Gulu lamphamvu.

Liri lochenjera,

Monga njokazo,

Pansi pa chizunzo,

Lipilirabe.

Limalemekeza

Yehova M’lungu;

Kulambira kwawo

kuwonjezeka.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena