Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 224
  • “Senzani Goli Langa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Senzani Goli Langa”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Goli Langa Lili Lofeŵa, ndi Katundu Wanga Ali Wopepuka”
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Yesu Ankatsitsimula Ena
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Mankhwala Omwe Angathandize Kuthetsa Nkhaŵa
    Nsanja ya Olonda—2001
  • “Bwerani kwa Ine . . . Ndipo Ndidzakutsitsimutsani”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 224

Nyimbo 224

“Senzani Goli Langa”

(Mateyu 11:28-30)

1. Inu otopetsedwa,

Ndi kupsinjika konse,

Yesu akuitana:

‘Idzanitu kwa ine.’

2. ‘Ine ndiri wofatsa,

Sindirinso wadziko.

Phunzirani kwa ine,

Mudzapeŵa muviwo.’

3. ‘Katundu ngwopepuka,

Ndi golilo nlofeŵa.

Ndipumulitsa mtima

Kwa onse olungama.’

4. Mukhaletu owona.

Adzakulimbitsani;

Muli m’goli limodzi,

Potumikira M’lungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena