Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsamba 7
  • Yesu Ankatsitsimula Ena

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yesu Ankatsitsimula Ena
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • “Goli Langa Lili Lofeŵa, ndi Katundu Wanga Ali Wopepuka”
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Mankhwala Omwe Angathandize Kuthetsa Nkhaŵa
    Nsanja ya Olonda—2001
  • “Bwerani kwa Ine . . . Ndipo Ndidzakutsitsimutsani”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • “Senzani Goli Langa”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2008
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 January tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MATEYU 10-11

Yesu Ankatsitsimula Ena

11:28-30

Mzimayi wa m’nthawi yakale atanyamula goli

“Goli langa ndi lofewa”

Popeza Yesu anali kalipentala, ankadziwa kupanga goli labwino ndipo mwina ankaika nsalu kapena chikopa kuti likhale lofewa. Pamene tinabatizidwa, tinasenza goli la Yesu ndipo tinakhala ophunzira ake. Pa nthawiyi tinasenza udindo waukulu komanso tinayamba kugwira ntchito yolalikira yomwe si yophweka. Komabe timasangalala kuchita zimenezi ndipo timapeza madalitso ambiri.

Kodi mwapeza madalitso otani kuyambira pamene munasenza goli la Yesu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena