Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 218
  • Ndi Kristu m’Paradaiso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndi Kristu m’Paradaiso
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mulungu Watilonjeza Paradaiso
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Watilonjeza Paradaiso
    Imbirani Yehova
  • “Tidzaonana M’Paradaiso”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • “Iwe Udzakhala ndi Ine m’Paradaiso”
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 218

Nyimbo 218

Ndi Kristu m’Paradaiso

(Luka 23:43)

1. Kristu ananena naye

‘Udzakhala m’paradaiso.’

Lonjezoli kwa wochimwa

Latisonkhezera

Chikhulupiliro.

Lipatsa chiyembekezo,

Mulungu achotsa imfa.

Chowonadicho tidziŵa.

Chiyanjo tipeza

Mu Baibulolo.

2. Khamu lalikulukulu

Lasunga chiyembekezo.

Silikhalanso mumantha.

Mawu a Mulu

ngu Amvekera bwino.

Tipempha modzichepetsa,

Timchitire utumiki

Ndi kumtamanda kosatha,

Mokhulupirika

Ndi chikondwerero.

3. “Nkhosa zina” zopambana

Zidzakhala m’paradaiso.

Izinso zizindikira

Ntchito za Mulungu!

Zochoka kwa iye.

Zilalikira Mbiriyo

Ndikusangalatsa anthu.

Njirayidi ndi ya nzeru;

Akhale ndi moyo

Mu paradaiso.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena