Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 63
  • Lolani Kuunika Kuŵale

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lolani Kuunika Kuŵale
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Muwalitse Kuunika Kwanu’
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2001
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 63

Nyimbo 63

Lolani Kuunika Kuŵale

(Mateyu 5:16)

1. M’lungu walamula

Kuti kuŵale

Akuchotsa mdima

wakale lomwe.

Kukachisi wake

Mphezi ziŵala,

Tikatsogozedwe

Ndi kuŵalako.

2. Mbiri ya Ufumu

Tilalikira

Kutonthoza onse

Akulirawo.

Mphamvu yofalitsa

Nja kwa Mulungu.

Ativumbulira

Za ntchito yathu.

3. Tithandizireni

Muutumiki,

Kutitu tisunge

Umphumphu wathu.

Ife anthu anu,

Mosangalala

Tidzalemekeza

Dzina loyera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena