Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 145
  • Khalani Woleza Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Woleza Mtima
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chipatso cha Mzimu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Njira Yoposa ya Chikondi
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 145

Nyimbo 145

Khalani Woleza Mtima

(1 Atesalonika 5:14)

1. N’kuleza mtima kotani

nanga Yehova asonyeza!

Nkana avutika apilira,

Samatopatu konse.

Anapilira ndi Israyeli,

Ndi mtundu wa’nthu onse.

Chotero nkhosa zonse zapeza

Kuleza mtima kwake.

2. Yehova Mulungu wamuyaya

Aleza mtima nafe,

Ndithudi okhulukidwa ife

Tisonyeze mkhalidwe.

Timafuna chipatso cha mzimu

Kutithandiza m’munda.

Kuti tisagonje ku choipa,

Tikhalebe ofatsa.

3. Kuleza mtima kutithandiza

Kusungabe umodzi

Mumpingotu ndiponso mubanja

M’lungutu akondwere!

Chikondi cha M’lungu chithandiza

Kuti tileze mtima.

Tikufuna kuti tipilire

Kufikira ungwiro.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena