Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 55
  • Kuyenda ndi Yehova Masiku Onse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuyenda ndi Yehova Masiku Onse
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Timayenda ndi Yehova Tsiku Lililonse!
    Imbirani Yehova
  • Tiziyenda ndi Yehova Tsiku Lililonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kristu Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Kodi Yehova Akufuna Chiyani kwa Ife?’
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 55

Nyimbo 55

Kuyenda ndi Yehova Masiku Onse

(Mika 6:8)

1. Timayenda ndi Yehova,

Masiku alionse.

Kukoma mtima kwakeko

Wapereka kwa anthu!

Pokhala ndi mwa kusankha

Kuyenda ndi Mulungu,

Tiyamba n’kudzipereka

Kuimira Mulungu.

2. Kuyendabe ndi Atate

Ndiko njira yanzeru.

Tazingidwa ndi adani

Angatilande mphotho.

Pali Satana n’ziwanda

Ndi misampha yathupi

Ndi chuma chadziko lino;

Zingakole mapazi!

3. M’lungu wapatsa thandizo

Kupyolera mwa mzimu,

Kupyola mwampingo wake,

Ndi mwa mapempherowo.

Poyendabe ndi Yehova,

Tichite choyenera.

Tikhaletu ndi chikondi

Ndipo odzichepetsa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena