Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 170
  • “Mulungu Akhale Wowona”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mulungu Akhale Wowona”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 170

Nyimbo 170

“Mulungu Akhale Wowona”

(Aroma 3:4)

1. Yehova ndiwacho’nadi;

Samanama konse.

Nthaŵi zonse timdalira;

Sangadzikanetu.

Iye alitu wowona

Munthu ndiwonama.

Cho’nadi chake chikhala

Kunthaŵi zosatha.

2. Pamene anatumiza

Mwana’ke padziko,

Yesu anasonyezabe,

Kuwona kwa M’lungu.

Chifuno cha Ya chinali,

Lamulo kwa iye.

Anakondwa m’choyenera

Natsogoza “nkhosa.”

3. Ngakhale anthu anyoza

Mawu a Mulungu,

Ife tisonyeza kuti;

M’lungu ndiwowona.

Tilalikira cho’nadi

Chokhala ndi mphamvu.

Tifuna cho’nadi chake,

Ndi kumvera M’lungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena