Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 20
  • Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 20

Nyimbo 20

Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu

(Salmo 96:1, 10)

1. Idzani, tiimbe nyimbo

Yaufumu m’dziko.

Imbitsitsani nyimboyo;

M’dziŵitse Ufumu.

Mapazi ovala mbiri

Akongola ndithu!

Nenani m’mitundu kuti,

‘Chilanditso ncha Ya.’

2. M’nyimbo yathu Yaufumu,

Titama Yehova.

Timamlambira mwamantha

Ndi kumudalitsa.

Mafano olambiridwa

Samapindulitsa.

Koma sitidzachoka kwa

M’lungu wa cho’nadi.

3. M’loŵe m’nyimbo Yaufumu:

“Yehova ndi Mfumu.”

Alamulira mwa Yesu;

Miyamba ikondwa.

Yehova adzaweruza

Dziko m’chilungamo,

Okhulupirika onse

Adzawadalitsa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena