Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 22
  • Kulabadira Uthenga wa Yuda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulabadira Uthenga wa Yuda
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Mulimbanetu Chifukwa cha Chikhulupiriro”!
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Tiyenera Kuchita Khama Kuti Tikhalebe m’Choonadi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Chenjerani ndi Ampatuko!
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Malangizo Okhudza Kukhala ndi Chikhulupiriro, Makhalidwe Abwino Ndiponso Chikondi
    Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 22

Nyimbo 22

Kulabadira Uthenga wa Yuda

(Yuda 21)

1. Timalimbikitsidwa

Ndi Mawu a Yuda.

Analembera ife

Kutitu tisagwe.

Uphungu wake wabwino

Utilimbikitsedi.

Udzatigalamutsa ndithu (mudzikoli).

2. Machenjezo amphamvu

Asonya choipa.

Satana ngwochenjera

Koma timdziŵadi.

Angatitayitse mphotho;

Mwamawudi onyenga,

Amayesa kutivulaza (tisamale)!

3. Mochenjera oipa

Angatinyengedi.

Tikusankha Mulungu,

Tisasocheretu.

Kutigalamutsa, mawu

A Yuda ngothandiza!

Choncho tidzapeŵa mpatuko (titerodi).

4. Inde, timenye nkhondo

Yachikhulupiro.

Chifundo, chikondi ndi

Mtendere zikule.

Kwa Yehova M’lungu wathu,

Mwa Yesu Mfumu yathu,

Tonse tipereke ulemu (kwa Yehova).

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena