Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 161
  • Pempherani kwa Yehova Tsiku ndi Tsiku

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pempherani kwa Yehova Tsiku ndi Tsiku
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Muzipemphera kwa Yehova Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse
    Imbirani Yehova
  • Yesu Atiphunzitsa Ife Kupemphera
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
  • Kodi Yehova Amamvetsera Mapemphero Athu?
    Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 161

Nyimbo 161

Pempherani kwa Yehova Tsiku ndi Tsiku

(1 Atesalonika 5:17)

1. Pempherani kwa Yehova Wathu.

Ndimwaŵi kukhala ndi dzinalo.

Tiri ndi ufulu wolankhula;

Ndiye Tate yemwe tingapemphe.

M’pempherebe kwa M’lungu.

2. Pempheranitu tsiku ndi tsiku,

Kumapempha chikhululukiro.

M’zonse timampempha chithandizo;

Amateteza sitidzawopa.

M’pempherebe kwa M’lungu.

3. Pempheranitu ngati zavuta.

Tingampatsetu mitima yathu,

Kumuuza nkhaŵa zathu zonse;

Iri tsono ndidalitso lathu.

M’pempherebe kwa M’lungu.

4. Pempheranitu m’kumathokoza.

Mtamandeni ndi kum’yamikira.

Lankhulani ndi Yehova mo’na,

Natidzawona ubwino wake.

M’pempherebe kwa M’lungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena