Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 85
  • Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndi Pothawira Pathu
    Imbirani Yehova
  • Yehova Ndi Pothawirapo Pathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu
    Nsanja ya Olonda—2001
  • ‘Pezani Chitetezo M’dzina la Yehova’
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 85

Nyimbo 85

Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu

(Salmo 91:1, 2)

1. Yehova pothaŵira,

Tidalira iye.

Mthunzi wakewo ndiwo;

Pobisala pathu.

Adzakupulumutsani

Kuchokera kumiliri.

Yehova ndiye linga,

Kwa olungama onse.

2. Nkana zikwi zidzagwa,

Pafupi ndi iwe,

Zikwi khumi kumanja;

Sudzavulazidwa.

Sudzagwedera ndi mantha,

Monga kuti nkuvulala.

Udzawona ndi maso,

Pokhala m’mapikomo.

3. Mliri sudzakugwera,

Ngakhaletu tsoka.

Mwa angelo Mulungu

Adzatchinjiriza.

Sudzawopa konse mkango;

Udzapondereza njoka.

Sudzakhumudwa konse

Potumikira M’lungu.

4. Ka’mba ka chidaliro;

Tamani Yehova.

Podziŵitsa ubwino,

Tipeŵa chitonzo.

Tidzipereke kwa M’lungu;

Adzatipulumutsatu.

Yehova pothaŵira,

Dzina lake ndi linga.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena