Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 95
  • Chipatso cha Ubwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chipatso cha Ubwino
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mbali Yodabwitsa ya Ubwino wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1989
  • “Ubwino Wake Ndi Waukulu Kwambiri!”
    Yandikirani Yehova
  • Ubwino Waukulu wa Yehova
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Yehova Ndiye Chitsanzo Chachikulu Pankhani Yosonyeza Ubwino
    Nsanja ya Olonda—2002
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 95

Nyimbo 95

Chipatso cha Ubwino

(Agalatiya 5:22)

1. Yehova ndiye Mfumu yamuyaya,

Ubwino chifundo mkhalidwe wake.

Anatumiza Mwana Kristu Yesu

Kuti asonyeze anthu kulapa.

2. Anthu athandizidwa ndi ubwino

Kumasulidwa kuchoka m’Babulo.

Mulungu atipatsa kuunika,

Kupatula chabwino ku choipa.

3. Ubwino wa M’lungu tiutsanzire;

Chipatso cha mzimu tichikulitse.

Tikhale aufulu m’chilungamo,

Kudalira M’lungu ndi Kristu Yesu.

4. Kukula mu’bwino tidzachitanji?

Kuphunzira kupemphera ndi ntchito.

Osaleka kusonkhana n’abale

Tidzakhala okhoza mu ubwino.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena