Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 29
  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yendani ndi Mtima Wosagawanika
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kuchita Zinthu Mokhulupirika
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuyenda Muumphumphu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yendani mu Umphumphu
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Kodi Mudzasungabe Umphumphu?
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 29

Nyimbo 29

Yendani ndi Mtima Wosagawanika

Losindikizidwa

(Salmo 26)

1. Mundiweruzetu Mbuye wanga;

Onani kuti ndimakudalirani.

Ndisanthuleni ndi kundiyesa;

Konzani mtima wanga, mundidalitse.

(KOLASI)

Koma ine, Ndatsimikizadi

Kusonyeza mtima Wosagawanika

2. Sindikhala pa anthu achabe.

Ndidana ndi anthu onyoza cho’nadi.

Musandichotsetu ndi ochimwa

Kapena ndi anthu okonda ziphuphu.

(KOLASI)

Koma ine, Ndatsimikizadi

Kusonyeza mtima Wosagawanika

3. Ndikonda kukhala m’nyumba yanu.

Ndidzachirikiza kulambira kwanu.

Ndidzayendadi kuguwa lanu,

Pokuyamikani mokweza kwambiri.

(KOLASI)

Koma ine, Ndatsimikizadi

Kusonyeza mtima Wosagawanika

(Onaninso Sal. 25:2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena