Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 8
  • Mgonero wa Ambuye

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mgonero wa Ambuye
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 8

Nyimbo 8

Mgonero wa Ambuye

Losindikizidwa

(Mateyo 26:26-30)

1. Atate wathu wakumwamba,

Usikuwu n’ngwapadera!

Pa Nisani fotini panaoneka

Chikondi, nzeru ndi mphamvu.

Mwanawankhosa anadyedwa,

Is’raeli namasuka.

Kenako Mbuye anakhetsa magazi

Kukwaniritsa ulosiwo.

2. Tasonkhana pamaso panu.

Tadza ngati nkhosa zanu

Kukutamandani pa chikondi chanu,

Dzina lanu tilikweze.

Tisunge Chikumbutso ichi,

m’mitima ndi m’maganizo.

Tidzamutsatira Khristu nthawi zonse

Kuti tidzaupeze moyo.

(Onanino Luka 22:14-20; 1 Akor. 11:23-26.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena