Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 15
  • Zolengedwa Zimasonyeza Ulemerero wa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zolengedwa Zimasonyeza Ulemerero wa Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Chilengedwe Chivumbula Ulemelero wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyenyezi Zilidi ndi Uthenga Wanu!
    Galamukani!—1994
  • Miyamba Imalengeza Ulemelero wa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyenyezi ndi Munthu—Kodi Pali Kugwirizana?
    Galamukani!—1994
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 15

Nyimbo 15

Zolengedwa Zimasonyeza Ulemerero wa Yehova

Losindikizidwa

(Salmo 19)

1. Yehova inetu ndimadziwa

Zamlengalenga ndi zodabwitsa.

Zimalemekeza dzina lanu

Ngakhale sizitulutsa mawu.

Zimalemekeza dzina lanu

Ngakhale sizitulutsa mawu.

2. Munalenga nyenyezi ndi dzuwa,

Munaika malire a nyanja.

Munalenga zinthu zodabwitsa

Komabe mumatiganizira.

Munalenga zinthu zodabwitsa

Komabe mumatiganizira.

3. Malamulo anu ndi oyera

Ndipo moyo amabwezeretsa.

N’ngofunika kuposa golide,

Tiwasungedi tiwatsatire.

N’ngofunika kuposa golide,

Tiwasungedi tiwatsatire.

(Onaninso Sal. 12:6; 89:7; 144:3; Aroma 1:20.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena