Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 31
  • Ndife Mboni za Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndife Mboni za Yehova!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Ndife Mboni za Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ndife Mboni za Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chuma Chapadera
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 31

Nyimbo 31

Ndife Mboni za Yehova!

Losindikizidwa

(Yesaya 43:10-12)

1. Asema timilungu,

M’lungu wo’na sam’dziwa.

Ndiwamphamvuyonse

Monga tiona.

Milunguyo sidziwa

Zinthu zili m’tsogolo.

Milunguyinso si yoona

Ndipo ilibenso mboni.

(KOLASI)

Mboni za Yehovafe

Tinena mosaopa.

M’lungu wathu akalosera

Zinthu zimachitika.

2. Tilalikire dzina

La Yehova Mulungu.

Ndi Ufumu wake

Molimba mtima.

Ena amve cho’nadi

Kuti chiwamasule.

Akamalimba, adzaimba

Kutamanda nafe M’lungu.

(KOLASI)

Mboni za Yehovafe

Tinena mosaopa.

M’lungu wathu akalosera

Zinthu zimachitika.

3. Ntchito yolalikira

Za dzina la Yehova.

Imachenjezadi

Olidetsawo.

Imathandiza anthu

Kukhululukidwadi.

Imabweretsanso chimwemwe,

Ndiponso chiyembekezo.

(KOLASI)

Mboni za Yehovafe

Tinena mosaopa.

M’lungu wathu akalosera

Zinthu zimachitika.

(Onaninso Yes. 37:19; 55:11; Ezek. 3:19.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena