Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 109
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Mwana Woyamba Kubadwa wa Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Ufumu wa Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 109

Nyimbo 109

Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova!

Losindikizidwa

(Aheberi 1:6)

1. Tamandani Yesu

Mfumu yodzozedwayo.

Yokonda choonadi

Komanso chilungamo.

Popereka ulemu

Ku dzina la M’lungu,

Ulamuliro wake

Adzalengezatu.

(KOLASI)

Tamandani Yesu!

Wodzozedwa wa M’lungu.

Anakhazikitsidwa

Pampando monga Mfumu!

2. Tamandani Yesu

Yemwe anatifera.

Anapereka dipo.

Ndithu n’ngodzichepetsa.

Mkwatibwi wake pano

Akudikirira.

Ukwati n’ngwakumwamba

Udzatidalitsa.

(KOLASI)

Tamandani Yesu!

Wodzozedwa wa M’lungu.

Anakhazikitsidwa

Pampando monga Mfumu!

(Onaninso Sal. 2:6; 45:3; Chiv. 19:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena