Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 130
  • Moyo Ndi Wodabwitsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo Ndi Wodabwitsa
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 130

Nyimbo 130

Moyo Ndi Wodabwitsa

Losindikizidwa

(Salimo 36:9)

1. Makanda onse, ndiponso mvula,

Mbewu komanso kuwala kwa dzuwa—

Ndizodabwitsa, zonse ndi mphatso.

Zimatithandiza kukhala ndi moyo.

(KOLASI)

Choncho tichitenji ndi mphatso iyi?

Tikonde Mulungu yemwe anatipatsa.

Sitingaipeze mphatsoyi patokha,

Mphatsoyi ya moyo ndi yodabwitsadi.

2. Ena ’ngasiye kulimba mtima

N’kunena kuti: ‘Kuli bwino kufa.’

Koma ifeyo sitili choncho.

Timayamikira kukhala ndi moyo.

(KOLASI)

Choncho tichitenji ndi mphatso iyi?

Tikonde anzathu amene tili nawo.

Sitingaipeze mphatsoyi patokha,

Mphatsoyi ya moyo ndi yodabwitsadi.

(Onaninso Yobu 2:9; Sal. 34:12; Mlal. 8:15; Mat. 22:37-40; Aroma 6:23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena