Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 106
  • Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tikhale pa Ubwenzi Ndi Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Akukuitanani Kuti Mukhale Bwenzi Lake
    Mungathe Kukhala Bwenzi la Mulungu!
  • Yehova—Kodi Ndimnansi Wanu Kapena Bwenzi Lanu?
    Nsanja ya Olonda—1992
  • Kodi Nchifukwa Ninji Sindimakhala ndi Mabwenzi?
    Galamukani!—1996
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 106

Nyimbo 106

Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova

Losindikizidwa

(Salimo 15)

1. Ndani angakhale

Bwenzi lanu M’lungu?

Ndani mungakhulupirire,

Angakhale nanu?

Ndi onse amene

Amakukondani,

Amakukhulupirirani,

Okonda cho’nadi.

2. Ndani angakhale

Bwenzi lanu M’lungu?

Ndani angafike

Kumpando wanu wachifumu?

Ndi onse

Amene amakumverani,

Olemekeza dzina lanu,

Okulambirani.

3. Timakuuzani

Zamumtima mwathu,

Ndipo timamva

Kuti tili pafupidi nanu.

Ndi inu tifuna

Kukhala mabwenzi.

Palibiretu bwenzi

Lomwe lingakuposeni.

(Onaninso Sal. 139:1; 1 Pet. 5:6, 7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena