Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 127
  • Malo Odziwika ndi Dzina Lanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malo Odziwika ndi Dzina Lanu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Malo Odziwika Ndi Dzina Lanu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 127

Nyimbo 127

Malo Odziwika ndi Dzina Lanu

Losindikizidwa

(1 Mbiri 29:16)

1. Yehova kukumangirani

Nyumbayi ndi mwayi wathu.

Tikuipereka tsopano

Lidziwike dzina lanu.

Zimene tingakupatseni

Zinalitu kale zanu.

Luso, ntchito ndi chuma chathu

Timakupatsani inu.

(KOLASI)

Tikupereka malowa

Kuti mudziwikedi.

Tikupereka malowa

Chonde alandireni.

2. Tikulemekeza inuyo

Pokutamandani pano,

Landirani ulemerero

Tikamachuluka muno.

Malowa tikukupatsani

Tidzawasamalirabe.

Ndipo apereke umboni

Inde mpaka kalekale.

(KOLASI)

Tikupereka malowa

Kuti mudziwikedi.

Tikupereka malowa

Chonde alandireni.

(Onaninso 1 Maf. 8:18, 27; 1 Mbiri 29:11-14; Mac. 20:24.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena