Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 47
  • Lalikirani Uthenga Wabwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lalikirani Uthenga Wabwino
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Lengezani Uthenga Wabwino
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Lengezani Mbiri Yabwino Yosatha
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chuma Chapadera
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Chifukwa Chake Tiyenera Kudziwa Dzina la Mulungu
    Dzina la Mulungu Limene Lidzakhala Kosatha
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 47

Nyimbo 47

Lalikirani Uthenga Wabwino

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 14:6, 7)

1. Poyamba sitinkadziwa za Ufumu.

Pano tikudziwa Mbewu yalonjezo.

Mwa chifundo ndi chikondi cha Yehova,

Anaganizira anthu ochimwafe.

Anakonza zoti Yesu alamule.

Ufumuwo unali woti udzabadwe.

Komanso kusankha kagulu ka nkhosa

Kadzakhale mkwatibwi wa Mwana wake.

2. Mulungu ankadziwa za uthengawu.

Tsopano afuna anthu audziwe.

Angelo amakondwa potithandiza

Kuchita ntchito yolengeza Ufumu.

Tilitu ndi udindo ndiponso mwayi

Wom’tamanda ndi kuyeretsa dzina lake.

Tili ndi mwayi wolengeza dzinalo

Mwa kulalikira uthenga wabwino.

(Onaninso Maliko 4:11; Mac. 5:31; 1 Akor. 2:1, 7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena