Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 81
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 81

Nyimbo 81

“Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

Losindikizidwa

(Luka 17:5)

1. Yehova nthawi zonse timachimwa

Chifukwa cha kupanda ungwiro.

Pali tchimo lomwe limatikola,

Kusowa kwa chikhulupiriro.

(KOLASI)

M’tiwonjezere chikhulupiriro.

Muzofo’ka zathu m’tithandize.

M’tiwonjezere mwachifundo chanu,

Tikulemekezeni mu zonse.

2. N’zosatheka kukukondweretsani

Ngati sitimakhulupirira.

Chikhulupiriro n’chotiteteza

Ndipo chimatilimbitsa mtima.

(KOLASI)

M’tiwonjezere chikhulupiriro.

Muzofo’ka zathu m’tithandize.

M’tiwonjezere mwachifundo chanu,

Tikulemekezeni mu zonse.

(Onaninso Gen. 8:21; Aheb. 11:6; 12:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena