Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 93
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Muzionetsa Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Muwalitse Kuunika Kwanu’
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2001
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 93

Nyimbo 93

“Onetsani Kuwala Kwanu”

Losindikizidwa

(Mateyu 5:16)

1. Yesu walamula kuti tiwale,

Ngati dzuwa kuti onse aone.

Mawu a Mulungu apatsa nzeru.

Tionetse kuwala ndi ntchito zathu.

2. Uthenga wabwino umawalitsa

Mitima ya anthu, n’kuwatonthoza.

Kuwala kwa Mawu a M’lungu wathu

Kumatitsogolera mu ntchito yathu.

3. Dziko limawala ndi mawu athu,

Limawalirabe ndi ntchito zathu.

Pochita zabwino tidzawalabe.

Mulungu pomaona asangalale.

(Onaninso Sal. 119:130; Mat. 5:14, 15, 45; Akol. 4:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena