Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 October tsamba 6
  • Yesetsani Kukhala Mwamtendere ndi Ena

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yesetsani Kukhala Mwamtendere ndi Ena
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Funafunani Mtendere ndi Kuulondola’
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Yesetsani Kukhala pa Mtendere ndi Ena
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Mmene Mungakumanire ndi Mtendere wa Umulungu Mokwanira Kwambiri?
    Nsanja ya Olonda—1987
  • “Titsatire Zinthu Zodzetsa Mtendere”
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 October tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MIYAMBO 17-21

Yesetsani Kukhala Mwamtendere ndi Ena

Mlongo akupemphera kenako akulankhula ndi mlongo wina yemwe anasemphana naye maganizo ndipo agwirizananso

Sikuti zimangochitika zokha kuti anthu a Yehova azikhala mwamtendere. Iwo akhoza kusemphana maganizo ndipo nthawi zina zimakhala zovuta kuti asakwiyirane. Koma malangizo a m’Baibulo amawathandiza kwambiri kuti akhazikitsenso mtendere.

Akhristu akasemphana maganizo amayesetsa kukhala mwamtendere ndipo . . .

19:11

  • amakhala odekha

18:13, 17

  • amayesetsa kuti adziwe nkhani yonse asanachite chilichonse

17:9

  • amasonyeza chikondi pokhululukira munthu amene wawalakwira

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena