Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 14
  • Tikukuthokozani Chifukwa cha Dipo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikukuthokozani Chifukwa cha Dipo
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Tikuthokoza Chifukwa cha Dipo
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Chimwemwe Chosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 14

Nyimbo 149

Tikukuthokozani Chifukwa cha Dipo

(Luka 22:20)

  1. Lero tabweratu,

    kwa inu Yehova,

    Chifukwa munatisonyezadi

    chikondi.

    Munapereka Mwana,

    wanu woyamba.

    Monga nsembe yoposa ina

    iliyonse.

    (KOLASI)

    Anafera anthu onse.

    Kuti tidzapulumuke.

    Tikuthokoza ndi mtima wonse,

    Inu M’lungu.

  2. Mofunitsitsa Yesu

    anapereka.

    Nsembe ya dipo moti

    tikusangalala.

    Asanabwere

    kudzatipulumutsa.

    Sitinkayembekezera,

    moyo wosatha.

    (KOLASI)

    Anafera anthu onse.

    Kuti tidzapulumuke.

    Tikuthokoza ndi mtima wonse,

    Inu M’lungu.

(Onaninso Aheb. 9:​13, 14; 1 Pet. 1:​18, 19.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena