Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 April tsamba 4
  • Kodi Muli ndi “Mtima Wodziwa” Yehova?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Muli ndi “Mtima Wodziwa” Yehova?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Zipatso—Zabwino ndi Zoipa
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Kodi Muli Ndi “Mtima Wodziwa” Yehova?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Munthu Aliyense Adzakhala Patsinde pa Mkuyu Wake
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Amosi Kodi Anali Wotchera Nkhuyu Kapena Wobaya Nkhuyu?
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 April tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 22-24

Kodi Muli ndi “Mtima Wodziwa” Yehova?

Kabasiketi kamene muli nkhuyu zabwino komanso ka basiketi kamene muli nkhuyu zoipa

Yehova anayerekezera anthu ndi nkhuyu

24:5

  • Ayuda okhulupirika omwe anali ku Babulo anali ngati nkhuyu zabwino

24:8

  • Mfumu Zedekiya komanso Ayuda ena osakhulupirika amene ankachita zoipa anali ngati nkhuyu zoipa

Kodi tingatani kuti tikhale ndi “mtima wodziwa” Yehova?

24:7

  • Yehova angatipatse ‘mtima womudziwa’ ngati timaphunzira Mawu ake ndi kugwiritsa ntchito zimene timaphunzirazo

  • Tiyenera kudzifufuza moona mtima n’kusintha makhalidwe ndi zilakolako zoipa zomwe zingawononge ubwenzi wathu ndi Yehova

Dzifunseni kuti: Kodi ndili ndi “mtima wodziwa” Yehova? Nanga ndingatani kuti ndikhale nawo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena