Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 129
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kugwiritsitsa “Chiyembekezo Chachimwemwe”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 129

Nyimbo 129

Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu

Losindikizidwa

(Aheberi 6:18, 19)

1. Anthu akhala akuyenda mumdima

Ndipo sanapindule kanthu n’komwe.

Zadziwika kuti anthu ochimwa

Kuvutika sangakuchotse.

(KOLASI)

Tiyeni tiimbe mokondwera

Poti Ufumu wa M’lungu wafika!

Yesu adzachotsadi zoipa,

Chiyembekezochi n’chonga nangula.

2. Uthenga womwe ukumveka ndi woti:

“Tsiku la Mulungu layandikira.”

Anthu ake sadzamvanso chisoni

M’lungu wathu timuimbira.

(KOLASI)

Tiyeni tiimbe mokondwera

Poti Ufumu wa M’lungu wafika!

Yesu adzachotsadi zoipa,

Chiyembekezochi n’chonga nangula.

(Onaninso Hab. 1:2, 3; Sal. 27:14; Yow. 2:1; Aroma 8:22.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena