Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 November tsamba 7
  • Khalanibe Maso Pamene Zinthu Zasintha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalanibe Maso Pamene Zinthu Zasintha
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Khalanibe Maso
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Mboni Za Yehova—Gulu la Dzinalo
    Nsanja ya Olonda—1992
  • Vidiyo Yatsopano Yothandiza Poyambitsa Maphunziro a Baibulo
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Zimene Mungachite Zinthu Zikasintha
    Galamukani!—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 November tsamba 7

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Khalanibe Maso Pamene Zinthu Zasintha

Zinthu zipitirizabe kusintha, makamaka m’masiku otsiriza ano. (1 Akor. 7:31) Kaya zinthu zimene zasinthazo timaziyembekezera kapena ayi komanso kaya ndi zabwino kapena zoipa, zingathe kusokoneza kulambira kwathu ndiponso ubwenzi wathu ndi Yehova. Ndiye n’chiyani chingatithandize kuti tikhalebe maso pamene zinthu zasintha? Onerani vidiyo yakuti Anakhalabe Olimba Mwauzimu Atasamukira Kudera Lina, ndipo kenako yankhani mafunso otsatirawa:

Banja likuchita Kulambira kwa Pabanja pa nthawi imene akukonzekera kusamuka
  • Kodi m’bale wina anapereka malangizo otani kwa bambo amene tamuona m’vidiyoyi?

  • Kodi mfundo ya pa Mateyu 7:25 ikugwirizana bwanji ndi zimene zinachitikira banjali?

  • Kodi banjali linachita zotani pokonzekera kusamuka ndipo zimenezi zinawathandiza bwanji?

  • Kodi n’chiyani chinathandiza banjali kuti lizolowerane mosavuta ndi anthu a mumpingo komanso gawo latsopano?

Kodi ndi zinthu ziti zimene zasintha kwambiri pa moyo wanga posachedwapa?

Malinga ndi mmene zinthu zilili pa moyo wanga, kodi ndingagwiritsire ntchito bwanji mfundo zomwe ndaphunzira m’vidiyoyi?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena