Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 28
  • Tikhale pa Ubwenzi Ndi Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikhale pa Ubwenzi Ndi Yehova
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova
    Imbirani Yehova
  • Mulungu Akukuitanani Kuti Mukhale Bwenzi Lake
    Mungathe Kukhala Bwenzi la Mulungu!
  • Yehova—Kodi Ndimnansi Wanu Kapena Bwenzi Lanu?
    Nsanja ya Olonda—1992
  • Kodi Nchifukwa Ninji Sindimakhala ndi Mabwenzi?
    Galamukani!—1996
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 28

NYIMBO 28

Tikhale pa Ubwenzi Ndi Yehova

Losindikizidwa

(Salimo 15)

  1. 1. Ndani angakhale

    bwenzi lanu M’lungu?

    Ndani mungam’khulupirire,

    angakhale mnzanu?

    Ndi onse amene

    amakudziwani,

    Amakukhulupirirani,

    amakukondani.

  2. 2. Ndani angakhale

    bwenzi lanu M’lungu?

    Ndani angafike kumpando

    wanu wachifumu?

    Ndi onse amene

    Amakumverani,

    Olemekeza dzina lanu,

    Okulambirani.

  3. 3. Timakuuzani

    Zamumtima mwathu.

    Mumakhala nafe pafupi

    Mumatithandiza.

    Tikufunitsitsa

    Kukhala anzanu

    Ndipo palibe bwenzi

    Lomwe lingakuposeni.

(Onaninso Sal. 139:1; 1 Pet. 5:​6, 7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena