Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 133
  • Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
  • Achinyamata, Kodi Mukukonzekera Tsogolo?
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Lambirani Yehova mu Unyamata
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pezani Chimwemwe mwa Kukhala Wopatsa!
    Nsanja ya Olonda—2001
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 133

NYIMBO 133

Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata

Losindikizidwa

(Mlaliki 12:1)

  1. 1. Anyamata ndi atsikanafe

    Ndife ofunika kwa Mulungu.

    Tikamam’tumikira mwakhama

    Azitidalitsa nthawi zonse.

  2. 2. Timasonyeza chikondi chathu

    Tikamalemekeza makolo.

    Anthu ndi M’lungu amatikonda

    Ndipo timayandikira M’lungu.

  3. 3. Tizikumbukira M’lungu wathu.

    Tikonde choonadi kwambiri.

    Tikakhulupirika kwa iye

    Tizisangalatsa mtima wake.

(Onaninso Sal. 71:17; Maliro 3:27; Aef. 6:​1-3.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena