Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 78
  • Kuphunzitsa Mawu a Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuphunzitsa Mawu a Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Phunzitsani Mwachikondi Ngati Yesu
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kupanga Dzina Labwino ndi Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Penyererani Chiphunzitso Chanu Nthaŵi Zonse
    Nsanja ya Olonda—1999
  • “Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti”
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 78

NYIMBO 78

Kuphunzitsa Mawu a Mulungu

Losindikizidwa

(Machitidwe 18:11)

  1. 1. Tikamaphunzitsa anthu

    Timasangalala.

    Timapeza madalitso

    Ochuluka ndithu.

    Timatsanziratu Yesu

    Pophunzitsa ena

    Ndiponso timawathandiza

    Kukonda Mulungu.

  2. 2. Pamene tikuphunzitsa

    Tichite zabwino,

    Anthu onse aziona

    Kuwala kwa M’lungu.

    Timafufuza mwakhama

    Mawu a Mulungu.

    Pouza ena uthengawu

    Timadziphunzitsa.

  3. 3. M’lungu watipatsa zoti

    Tiziphunzitsira

    Ndipo tikamamupempha

    Adzatithandiza.

    Timakonda mawu ake

    Omwe ndi oona.

    Tizikonda anthu omwe

    Timawaphunzitsawo.

(Onaninso Sal. 119:97; 2 Tim. 4:2; Tito 2:7; 1 Yoh. 5:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena