Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 67
  • “Lalikira Mawu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Lalikira Mawu”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova
  • “Lalika Mawu”!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 67

NYIMBO 67

“Lalikira Mawu”

Losindikizidwa

(2 Timoteyo 4:2)

  1. 1. Mulungu watilamula

    Ndipo tikufunika kumvera.

    Tizifotokozera anthu

    Adziwe chiyembekezo chathu.

    (KOLASI)

    Lalikira,

    Indetu onse amve.

    Lalika

    Dzikoli lisanathe.

    Lalika

    Ofatsa amvetsere

    Lalika

    M’dziko lonse.

  2. 2. Mavuto adzatiyesa.

    Tingapezeke tikunyozedwa.

    Kulalikira kungavute.

    Tidzakhulupirirabe M’lungu.

    (KOLASI)

    Lalikira,

    Indetu onse amve.

    Lalika

    Dzikoli lisanathe.

    Lalika

    Ofatsa amvetsere

    Lalika

    M’dziko lonse.

  3. 3. Nthawi zina tizipeza

    Anthu ofuna kutimvetsera.

    Tiziwaphunzitsa mwakhama.

    Tiyeretse dzina la Yehova.

    (KOLASI)

    Lalikira,

    Indetu onse amve.

    Lalika

    Dzikoli lisanathe.

    Lalika

    Ofatsa amvetsere

    Lalika

    M’dziko lonse.

(Onaninso Mat. 10:7; 24:14; Mac. 10:42; 1 Pet. 3:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena