NYIMBO 25
Chuma Chapadera
Losindikizidwa
1. Odzozedwa ndi mtundu
Watsopano wa M’lungu.
Iye anawagula
Padziko lapansi.
(KOLASI)
Anthu odzozedwa
Ndi chuma chapadera.
Amakukondani.
Amalalikira za inu.
2. Ndi mtundu wapadera,
Wokonda choonadi.
M’lungu wawalandira
Mu kuwala kwake.
(KOLASI)
Anthu odzozedwa
Ndi chuma chapadera.
Amakukondani.
Amalalikira za inu.
3. Amasonkhanitsanso
Nkhosa zina mwakhama.
Ndi okhulupirika
Kwa Mwanawankhosa.
(KOLASI)
Anthu odzozedwa
Ndi chuma chapadera.
Amakukondani.
Amalalikira za inu.
(Onaninso Yes. 43:20b, 21; Mal. 3:17; Akol. 1:13.)