Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 25
  • Chuma Chapadera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chuma Chapadera
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Chuma Chapadera
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Ndife Mboni za Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Mwana Wake Wodzozedwa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 25

NYIMBO 25

Chuma Chapadera

Losindikizidwa

(1 Petulo 2:9)

  1. 1. Odzozedwa ndi mtundu

    Watsopano wa M’lungu.

    Iye anawagula

    Padziko lapansi.

    (KOLASI)

    Anthu odzozedwa

    Ndi chuma chapadera.

    Amakukondani.

    Amalalikira za inu.

  2. 2. Ndi mtundu wapadera,

    Wokonda choonadi.

    M’lungu wawalandira

    Mu kuwala kwake.

    (KOLASI)

    Anthu odzozedwa

    Ndi chuma chapadera.

    Amakukondani.

    Amalalikira za inu.

  3. 3. Amasonkhanitsanso

    Nkhosa zina mwakhama.

    Ndi okhulupirika

    Kwa Mwanawankhosa.

    (KOLASI)

    Anthu odzozedwa

    Ndi chuma chapadera.

    Amakukondani.

    Amalalikira za inu.

(Onaninso Yes. 43:20b, 21; Mal. 3:​17; Akol. 1:​13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena