Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 20
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 20

NYIMBO 20

Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha

Losindikizidwa

(1 Yohane 4:9)

  1. 1. Yehova tinali

    Opanda tsogolo,

    Komano dipo

    Lathandiza tonse.

    Tikudzipereka

    Kwa inu kosatha.

    Tiphunzitse anthu

    Akudziweninso.

    (KOLASI)

    Munaperekatu

    Mwana wanu yekha.

    Tidzakuimbirani,

    Za mphatsoyi mpaka kale.

  2. 2. Chikondi chanuchi

    Ndi chachikuludi

    Komanso mumatikomera

    Mtima.

    Yoposa zonsezi

    Ndi mphatso ya Yesu.

    Anatifera kuti

    Tipulumuke.

    (KOLASI)

    Munaperekatu 

    Mwana wanu yekha.

    Tidzakuimbirani,

    Za mphatsoyi mpaka kale.

    (KUMALIZA)

    Yehova, Atate, zikomo kwambiri.

    Tidzakumbukira mphatsoyi mpaka kale.

(Onaninso Yoh. 3:​16; 15:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena