Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 120
  • Tikhale Ofatsa Ngati Khristu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikhale Ofatsa Ngati Khristu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa
    Imbirani Yehova
  • Kufatsa​—Kodi N’kofunika Bwanji?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • Kufatsa Ndi Khalidwe Lachikristu Lofunika Kwambiri
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Onetsani ‘Kufatsa Konse pa Anthu Onse’
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 120

NYIMBO 120

Tikhale Ofatsa Ngati Khristu

Losindikizidwa

(Mateyu 11:​28-30)

  1. 1. Yesu anali munthu wapadera

    Koma sanadzikuze, sananyade.

    Anali ndi udindo wapamwamba

    Komatu anali wodzichepetsa.

  2. 2. Kwa anthu omwe ali ndi mavuto,

    Yesu walonjeza kuwathandiza.

    Akamaika Ufumu poyamba

    Iye aziwachitira chifundo.

  3. 3. Yesu anati: ‘Tonse ndi abale.’

    Timamumvera monga Mutu wathu.

    Ofatsa ndi ofunika kwa M’lungu,

    Adzalandira dziko latsopano.

(Onaninso Miy. 3:34; Mat. 5:5; 23:8; Aroma 12:16.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena