Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 18
  • Tikuthokoza Chifukwa cha Dipo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikuthokoza Chifukwa cha Dipo
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikukuthokozani Chifukwa cha Dipo
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Chimwemwe Chosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 18

NYIMBO 18

Tikuthokoza Chifukwa cha Dipo

Losindikizidwa

(Luka 22:20)

  1. 1. Tsopano tabwera

    Kwa inu Yehova

    Chifukwa munatisonyezadi

    Chikondi.

    Munapereka Mwana

    Wanu woyamba

    Monga nsembe yoposa ina

    Iliyonse.

    (KOLASI)

    Anafera anthu tonse

    Kuti tidzapulumuke.

    Tikuthokoza ndi mtima wonse

    Inu M’lungu.

  2. 2. Mofunitsitsa Yesu

    Anapereka

    Nsembe ya dipo ndipo

    Tikusangalala.

    Asanabwere

    Kudzapereka dipo,

    Sitinkayembekezera

    Moyo wosatha.

    (KOLASI)

    Anafera anthu tonse

    Kuti tidzapulumuke.

    Tikuthokoza ndi mtima wonse

    Inu M’lungu.

(Onaninso Aheb. 9:​13, 14; 1 Pet. 1:​18, 19.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena