Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 39
  • Tipange Mbiri Yabwino kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tipange Mbiri Yabwino kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Kupanga Dzina Labwino ndi Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chifukwa Chake Tiyenera Kudziwa Dzina la Mulungu
    Dzina la Mulungu Limene Lidzakhala Kosatha
  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kugwiritsa Ntchito Dzina la Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 39

NYIMBO 39

Tipange Mbiri Yabwino Kwa Mulungu

Losindikizidwa

(Mlaliki 7:1)

  1. 1. Tsiku ndi tsiku tiziyesetsabe

    Kupanga mbiri yabwino kwa M’lungu.

    Tikachita zomwe M’lungu amafuna

    Adzatikonda nthawi zonse.

  2. 2. Kufunitsitsa kutchuka m’dzikoli

    Cholinga choti anthu atikonde,

    Ndi kopanda phindu chifukwa Yehova

    Sangatikonde tikatero.

  3. 3. Tikufunadi kulembedwa dzina

    Kuti likhale mu buku la moyo.

    Choncho tizikhala ndi mbiri yabwino

    Kwa M’lungu wathu mpaka kale.

(Onaninso Gen. 11:4; Miy. 22:1; Mal. 3:16; Chiv. 20:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena