Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • bi12 tsamba 1942-1943
  • 4 Mzimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • 4 Mzimu
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
4 Mzimu

4 Mzimu

M’Malemba Achiheberi, mawu achiheberi akuti ruʹach (luwaki) akupezeka maulendo 260 kuyambira pa Ge 1:2. Mawuwa amatanthauza “mpweya umene munthu amatulutsa popuma,” koma alinso ndi matanthauzo ena kuwonjezera pamenepo. Matanthauzo onsewa akugwirizana pa mfundo imodzi iyi: Onse amanena za chinthu chosaoneka kwa anthu koma chimene chimasonyeza kuti pali mphamvu inayake imene ikugwira ntchito. Mphamvu yosaoneka imeneyo imatha kuchita zinthu zina zimene zimaoneka.

M’Malemba Achigiriki, mawu achigiriki akuti pneuʹma (penevuma) akupezeka maulendo 334, kuyambira pa Mt 1:18, pamene pakupezeka mawu akuti “mzimu woyera.” Mawu amenewa ndi ofanana matanthauzo ndi mawu achiheberi aja akuti ruʹach.

M’munsimu muli timitu tosiyanasiyana timene tikusonyeza malemba mmene mukupezeka mawu akuti ruʹach ndi pneuʹma.

Mphepo

Ge 8:1; Eks 10:13; 1Mf 18:45; Yoh 3:8.

Mzimu woyera, kapena Mphamvu ya Mulungu yogwira ntchito

Ge 1:2; 41:38; Nu 11:25; Owe 6:34; 1Sa 19:20; 2Mb 24:20; Yes 11:2; Eze 11:5; Zek 4:6; Mt 1:18; 28:19; Mko 1:8; Lu 1:67; 2:27; Yoh 14:26; Mac 1:8; 2:33; Aro 5:5; 8:15, 16; 2Ak 13:14; Aef 3:16; 4:4; 1At 5:19; Tit 3:5; Yuda 20.

Mphamvu ya moyo

Ge 6:17; Yob 27:3; 34:14; Sl 31:5; 146:4; Mla 3:19; 12:7; Yes 42:5; Lu 8:55; 23:46; Mac 7:59.

Mulungu ndi mzimu, kapena wauzimu

Yoh 4:24; 2Ak 3:17; 3:18.

Zolengedwa zauzimu

1Mf 22:21; Eze 3:12; 8:3; Mt 8:16; 10:1; Mko 3:11; 3:30; 1Ak 15:45; Ahe 1:7; 1Pe 3:18.

Kudzipereka, mtima, ndi maganizo

Ge 45:27; Eks 35:21; Nu 14:24; Yob 17:1; Miy 25:28; Yes 57:15; Da 2:1; Lu 1:17; Yoh 11:33; 13:21; Mac 17:16; 1Ak 16:18; 2Ak 2:13; 7:13; 1At 5:23.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena