Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sp tsamba 7
  • Yehova Analenga Angelo Ambirimbiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Analenga Angelo Ambirimbiri
  • Kodi Mizimu ya Akufa Ilipodi?
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Anthu Akafa Amasanduka Angelo?
    Galamukani!—2006
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Kodi Angelo Ndi Otani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Mmene Angelo Angakuthandizireni
    Nsanja ya Olonda—1998
Onani Zambiri
Kodi Mizimu ya Akufa Ilipodi?
sp tsamba 7

Yehova Analenga Angelo Ambirimbiri

Baibulo limanena kuti Yehova ndi mzimu. Iye analenganso angelo ambirimbiri omwe ali ndi matupi auzimu.​—Yohane 4:24; 2 Akorinto 3:17, 18.

Poyambirira, Yehova analipo yekha. Kenako anayamba kulenga angelo omwe ndi amphamvu komanso anzeru kuposa anthufe. Angelowa alipo ambirimbiri ndipo Danieli anaona m’masomphenya angelo okwana 100 miliyoni.​—Danieli 7:10; Aheberi 1:7.

Angelowa analengedwa dziko lapansili lisanalengedwe. (Yobu 38:4-7) Iwowa si anthu amene anamwalira padzikoli n’kupita kumwamba.

Angelo ali kutsogolo kwa mpando wachifumu wa Yehova

Yehova analenga angelo ambirimbiri

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena