Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 126
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • “Talawani Ndipo Muona Kuti Yehova Ndi Wabwino”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 126

Nyimbo 126

Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi

Losindikizidwa

(Salimo 127:1)

1. Yehova tikufuna

Kupemphera mokhudzidwa.

Chifukwa mwatikonda ndipo

Tasangalala.

Taona mwadalitsa

Ntchito imene tagwira,

Ndipo tamangadi nyumbayi,

Mwatithandiza.

(KOLASI)

Kukumangirani nyumbayi

Yehova unali mwayi.

Nthawi zonse tilemekeze dzina lanu

Ndi kukutumikirani.

2. Mabwenzi okondwera,

Taonani tawapeza.

Sitidzaiwala mpakana

M’moyo wosatha.

Taona mzimu wanu

Mukugwirizana kwathu.

Mwayi taupeza wokwezadi

Dzina lanu.

(KOLASI)

Kukumangirani nyumbayi

Yehova unali mwayi.

Nthawi zonse tilemekeze dzina lanu

Ndi kukutumikirani.

(Onaninso Sal. 116:1; 147:1; Aroma 15:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena